Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

 

’TATE wa Kumwambako,
Likayere Dzinalo,
Udzetu Ufumu wanu;
Chifuniro chanucho
Chichitike pansipa
Monga chachitika kwanu.

Mutipatse leroli
E, chakudya chathuchi
Tsiku n’tsiku tichilira.
Mukhululukiredi
Tchimo lathu, monga ’fe
Iwo adatichimwira.

Musatifikitsemo
Muli mayeserowo,
Koma mutipulumutse.
Wanu ndi ufumuwo,
Mphamvu ndi ulemunso
Kufikira nthaŵi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version