Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

 

’TATE wa Kumwambako,
Likayere Dzinalo,
Udzetu Ufumu wanu;
Chifuniro chanucho
Chichitike pansipa
Monga chachitika kwanu.

Mutipatse leroli
E, chakudya chathuchi
Tsiku n’tsiku tichilira.
Mukhululukiredi
Tchimo lathu, monga ’fe
Iwo adatichimwira.

Musatifikitsemo
Muli mayeserowo,
Koma mutipulumutse.
Wanu ndi ufumuwo,
Mphamvu ndi ulemunso
Kufikira nthaŵi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Next: Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version