Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,

 

POLUMIDWA ndi njokazo,
M’chipululumo;
Aisrayeli ‘nafa,
Ambiri.

Mwachikondi Mlungu “Tate,
Nawuza Mose:
“Yamkuwa njoka upange,
Msangatu.”

Amene akayang’ane,
Njoka pamtengo;
Ngakhaletu walumidwa,
Achira.

Satana amatiluma,
Ndi uchimowo;
Mwana Mlungu natifera,
Pamtanda.

Tiyang’ane pamtandapo,
Tipulumuke;
Adzatitenga kupita,
Kwawoko.

Post navigation

Previous: Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
Next: Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hello world!
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version