Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

 

ANTHU m’maiko onse
Akhala mitundu;
Kapena m’dziko lino
Akhala anzathu;
Agona mwa zoipa,
Apulukiradi,

Ati, Mutilangize
Abale, bwerani.

Ngakhale alemera
Ndi chuma cha dziko,
Kodi akakondwera
Opanda Mulungu?
Kodi akhala mwaŵi
Otsata zawozo?
Iyai, awonongeka,
Apeza tsokalo.

Ndi ife akudziŵa
Chikondi cha Mlungu,
Kodi tidzaŵamana
Kuŵala kwa Kristu?
Chipulumutso! Inde,
Tichibukitsetu,
Kuti mitundu yonse
Ibwere kwa Yesu.

Akristu nyamulani
Maneno a Mulunguyo,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse;
Ndi Mwana wa Mlungu.

Post navigation

Previous: Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
Next: Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version