Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 181 PANALITU wakudwala

  1. Home   »  
  2. Hymn 181 PANALITU wakudwala

Hymn 181 PANALITU wakudwala

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 181 PANALITU wakudwala

 

PANALITU wakudwala
Amene akakhala
Pakhomo la sunagoge:
Kuti anthu ena
Amuone iye.

Yenda iwe, yenda.
Yenda iwe, yenda,
Siliva ndilibe;
Mwa Yesuyo, yenda!

Kukondwa kwa wodwalayo
Kunali kopambana;
Iye anatumphatumpha,
Kuzungulira
Sunagoge yense.

Lero lino Mbuye Yesu
Aitana nonsenu;
Mukamvera ndi kumtsata,
Mudzakondwera
Ndi mdalitso wake.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version