Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

 

MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyeretsedwe m’mtimamu;
Mupatse anthu anuwa
Mitulo yanu yonseyo.

Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo,
Ndi kutidzutsa m’moyomu,
Tikhale okondanatu.

Pankhope pathu mthirepo
Chisomo chanu chijacho;
Mtendere mutininkhebe,
Mutiyendetse ponse phee!

Tionetseni tonsetu
Umodzi wanu wonsemo,
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu
Tiimbe Nthaŵi zonsezo:

Titamire Nthaŵi zonse
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse.
Amen

Post navigation

Previous: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
Next: Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version