Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

 

MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyeretsedwe m’mtimamu;
Mupatse anthu anuwa
Mitulo yanu yonseyo.

Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo,
Ndi kutidzutsa m’moyomu,
Tikhale okondanatu.

Pankhope pathu mthirepo
Chisomo chanu chijacho;
Mtendere mutininkhebe,
Mutiyendetse ponse phee!

Tionetseni tonsetu
Umodzi wanu wonsemo,
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu
Tiimbe Nthaŵi zonsezo:

Titamire Nthaŵi zonse
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse.
Amen

Post navigation

Previous: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
Next: Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version