Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
Next: Hymn 274 YESU and’itana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version