Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
Next: Hymn 274 YESU and’itana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version