Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
Next: Hymn 274 YESU and’itana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version