Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,

 

USAFUNE chuma chokha,
Pena masewero okha;
Koma za Mulungu zokha,
Zipambana zinazo.

Ukafuna kulemera,
Pempha chuma chosathera;
Ndiwo mtima wakuyera,
Ndi wokonda Yesuyo.

Zosawutsa uvomere,
Ndipo Yesu chaulere;
Chikondano ndi mtendere,
Alowetsa m’mtimamo.

Zonse umazinyadira,
Udzaleka kusilira;
Uli nazo zokwanira,
Pakupeza Yesuyo.

Mbiri yake ubukitse,
Anthu onse nuphunzitse;
Kwa Mulungu nufikitse,
Osokera onsewo.

Yesu sakusiya konse,
Mphamvu, nzeru, chuma chonse;
Akupatsa nsiku zonse,
Tsata Yesu yekhayo.

Post navigation

Previous: Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
Next: Hymn 274 YESU and’itana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version