Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

 

NDISAUKA, ndinachimwa,
Koma Inu m’nandifera;
Ndimo ndamva mund’itana,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, ndimasowa,
Mphamvu yakuyera m’mtima;
Mwazi wanu wanditsuka,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindikhoza,
Kuiletsa nkhondo m’ mtima;
Ndi chisoni, mantha nkhawa,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindiona,
Ndingodwala, ndilefuka;
Zonse ndizitaya kwa ‘Nu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mulandira,
Muchiritsa, m’ pulumutsa;
Mawu anu ndivomera,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mundikonda,
Zonse zina ndazitaya;
Tsono kukhala wanu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Post navigation

Previous: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
Next: Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version