Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

 

NDISAUKA, ndinachimwa,
Koma Inu m’nandifera;
Ndimo ndamva mund’itana,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, ndimasowa,
Mphamvu yakuyera m’mtima;
Mwazi wanu wanditsuka,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindikhoza,
Kuiletsa nkhondo m’ mtima;
Ndi chisoni, mantha nkhawa,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindiona,
Ndingodwala, ndilefuka;
Zonse ndizitaya kwa ‘Nu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mulandira,
Muchiritsa, m’ pulumutsa;
Mawu anu ndivomera,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mundikonda,
Zonse zina ndazitaya;
Tsono kukhala wanu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Post navigation

Previous: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
Next: Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version