Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 282 INU muli mehere,
Next: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version