Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 282 INU muli mehere,
Next: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version