Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

 

TITAME Mlungu Wakumwamba,
Timwimbire nyimbo,
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo.

(Timwimbire nyimbo,
Timwimbire nyimbo!
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo)

Poyamba paja analenga
Zonse dziko muno,
Tsopano lomwe azisunga
Zonse zili moyo.

Tinasokera ngati nkhosa,
Moyo tinataya,
Tinakondwera ndi zoipa
Zonse tinatsata.

Komweko titasaukira,
Titafuna kufa,
Atate anatilondola
Naitana ife.

Tiyeni tizipita kwathu,
Tisasokerenso,
Tilape m’mtima kuti
tikakhale ndi Mulungu.

Post navigation

Previous: Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
Next: Hymn 25 ANGELO amayimba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version