Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

 

TITAME Mlungu Wakumwamba,
Timwimbire nyimbo,
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo.

(Timwimbire nyimbo,
Timwimbire nyimbo!
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo)

Poyamba paja analenga
Zonse dziko muno,
Tsopano lomwe azisunga
Zonse zili moyo.

Tinasokera ngati nkhosa,
Moyo tinataya,
Tinakondwera ndi zoipa
Zonse tinatsata.

Komweko titasaukira,
Titafuna kufa,
Atate anatilondola
Naitana ife.

Tiyeni tizipita kwathu,
Tisasokerenso,
Tilape m’mtima kuti
tikakhale ndi Mulungu.

Post navigation

Previous: Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
Next: Hymn 25 ANGELO amayimba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version