Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

 

TIYENI, Akristu inu,
Mumenyane nkhondo iyi,
Mukafoka nonse, koma
Yesu akulimbitsani.

Muyendanso kunka komwe,
Mugonjetse mdani wanu;
Musafoke, musaleme,
Musagone konse inu.

Musagonje, anthu inu,
Mtamiretu Yekha Mbuye;
Ipambana mphamvu yake,
Ya Mtsogoli wanu yemwe.

Mtima wanu wonse ndithu
Udzakhala ndi chimwemwe.
Zida zanu mbvale bwino
Zakudzera m’Mwamba momwe.

Limbikani inu nonse,
Msangalalo ngwanu nokha;
Musaope kanthu kena
Mumtamire Mbuye Yekha.

Tiyeni ku nkhondo iyi,
Mugonjetse zonse konko;
Muingitse mdani uja,
Muyendetse m’njira momwemo.

Post navigation

Previous: Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Next: Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version