Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

 

PAPHIRI ndi padambo,
Ponsepo pali Mlungu;
Poyenda ife m’njira,
MpoYima pali Mlungu.
Kokwera Maganizo,
Komwe kuli Mlungu;
Kumwamba ndi pansipo,
Ponsepo pali Mlungu.

(Mulungu ali nane!)
(Ali nane, ali nane,
ali nane, ali nane, Aa!
Mulungu ali nane!)

Ndi maso Ambuyathu,
Apenyetsetsa ife;
Amadalitsa onse,
Okhulupi’ra Iye.
Amamva timbalame,
Naveka dziko lonse;
Sataya tizirombo,
Asunga zina zonse.

Okwaŵa pansi inu,
Oyenda m’madzi inu;
Oyesa dziko n’kwanu,
A m’mlengalenga inu.
Nonsenu ntchito zake,
Muwona tsiku n’tsiku;
Saleka kusamala,
Ndikudalitsa inu.

Nditama mphamvu yake,
Ya Mlungu yondizinga;
N’kafoka andilimbitsa,
N’kadwala andichiza.
Pakundisiya bwenzi,
Mulungu ali paja;
N’kaloŵa imfa ine,
Alipo Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
Next: Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 491 N’takafika kwanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version