Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

 

PAPHIRI ndi padambo,
Ponsepo pali Mlungu;
Poyenda ife m’njira,
MpoYima pali Mlungu.
Kokwera Maganizo,
Komwe kuli Mlungu;
Kumwamba ndi pansipo,
Ponsepo pali Mlungu.

(Mulungu ali nane!)
(Ali nane, ali nane,
ali nane, ali nane, Aa!
Mulungu ali nane!)

Ndi maso Ambuyathu,
Apenyetsetsa ife;
Amadalitsa onse,
Okhulupi’ra Iye.
Amamva timbalame,
Naveka dziko lonse;
Sataya tizirombo,
Asunga zina zonse.

Okwaŵa pansi inu,
Oyenda m’madzi inu;
Oyesa dziko n’kwanu,
A m’mlengalenga inu.
Nonsenu ntchito zake,
Muwona tsiku n’tsiku;
Saleka kusamala,
Ndikudalitsa inu.

Nditama mphamvu yake,
Ya Mlungu yondizinga;
N’kafoka andilimbitsa,
N’kadwala andichiza.
Pakundisiya bwenzi,
Mulungu ali paja;
N’kaloŵa imfa ine,
Alipo Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
Next: Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version