Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

 

NDITAMATU Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko lakumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindizaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Pa dziko pano pena m’Mwambamo.

Ndiye wokondwa, E, munthuyo,
Wokhulupirira Mlungu yekhadi;
Wolenga dziko, nyanja, zonsezi.
Choona chake chonse chingokhalatu chosatha,
Apulumutsa onse namadyetsa anthu akewo;
Wokonda ndiye Mlungu wathuyo.

Mlungu kuwona athiratu,
Inde m’maso awo osapenyawo;
Natuma akumvera mpumulo.
Amathandiza inde aulendo awo ofokatu,
Akazi amasiye, maka ndi ana’wo onsewo;
Olira otonthoza mtimadi.

Nditama Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko la Kumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindidzaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Padziko pano pena m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
Next: Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version