Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

  1. Home   »  
  2. Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

 

POKONDWA ndi poona vuto
Ndi tsoka pena mwayi,
Ndikumbukira, ndiimbira
Mulungu wangayo.

Kwezani nane Ambuyathu,
Timlemekeze yekha;
Popsinja mtima ndinamtchula,
Nandithangata ’ne

Angelo amazinga nyumba
Za anthu olungama;
Mulungu ateteza omwe
Amkhulupirira.

Laŵani chikondano chake;
Mudzadziŵitsa msanga
Kudala kwawo kwa anake
Omkonda Mbuyeyo.

Opani iye, nimuleke
Kuopa kanthu kena;
Mumtumikire mokondwera,
Akusungani ’nu.

Mulungu wathu Mmodzi yekha
Atate, Mwana, Mzimu,
Akhale ndi ulemerero
Wachikhalirewo!

Post navigation

Previous: Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
Next: Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version