Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

 

LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
Musekerere kuti tidzaimbira Yesu.
Imbira!
Timwimbire Yesu,
Mpulumutsi wathu!

Imbira!
Timwimbire Yesu,
Tonse tidzakondwera.

Musadziunjikire chuma cha padziko
Dzimbiri ndi njenjete
zimachiononga.

Koma mudziunjikire chuma cha Kumwamba
Kumene anapita Mtsogoleri wanu.

Aliponso adani am’kati ndi akunja;
Yesu watisekera, tidzakuimbirani.

Aliponse mabvuto, ena ndi oipa;
Yesu mutimasule kwa adani athu.

Post navigation

Previous: Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
Next: Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version