Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.

  1. Home   »  
  2. Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.

Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.

 

MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
Kalata ilozera njira;
Amaitanatu tonsefe,
Bvomerani Iye.

Tidzakondweradi m’Mwambamo
Posonkhana komwe kuli ’Ye;
Tidzakhala naye komweko
Ku Dziko losafa.

Lolani ana, mumve Mlungu,
Tsegulani mitima yanu,
Sankhani Iye, Bwenzi lanu;
Musachedwe, mudze.

Ganizansoni, ali pano,
Mthenga wake mverani lero;
Mawu okoma ati lero,
Musachedwe, mudze.

Post navigation

Previous: Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
Next: Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version