Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

 

AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Nanga inu? Nanga inu?
Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

Masiku onse timakondwera
Pakumva Mawu ake a Yesu;
Wolalikira tidzamumvera;
Nanga inu?

Ife tiyembekezera YESU,
Nanga inu? Nanga inu?
Chimwemwecho chilimumtimamu;
Nanga inu?

Titasokera tinabwerera,
Nanga inu? Nanga inu?
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo;
Nanga inu?

Tinachoka munjira ya imfa,
Nanga inu? Nanga inu?
Takopeka ndi Mawu a Yesu;
Nanga inu?

Post navigation

Previous: Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
Next: Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version