Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

 

AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Nanga inu? Nanga inu?
Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

Masiku onse timakondwera
Pakumva Mawu ake a Yesu;
Wolalikira tidzamumvera;
Nanga inu?

Ife tiyembekezera YESU,
Nanga inu? Nanga inu?
Chimwemwecho chilimumtimamu;
Nanga inu?

Titasokera tinabwerera,
Nanga inu? Nanga inu?
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo;
Nanga inu?

Tinachoka munjira ya imfa,
Nanga inu? Nanga inu?
Takopeka ndi Mawu a Yesu;
Nanga inu?

Post navigation

Previous: Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
Next: Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version