Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

 

AKRISTU limbikani,
Imani mtima nji!
Mbendera nyamulani,
Msatenthemere ’yi.
Wotsogolera wathu
Ndi Mwana wa Mulungu;
Adzagonjetsa onse
Adani athuwo.

Tigwire nkhondo yomwe
Ya Mbuye wathuyo;
Tileke zakuipa
Zokhala m’mtimamo.
Sitikwanira tokha
Kuleka zathu zomwe,
Koma Mbuyathu Yesu
Atithangatatu.

Tsopano timenyana
Ndi zakuipazi;
Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
Yesu adzalandira
Ankhondo ake onse;
Adzakhalika naye
Kumwamba komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version