Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

 

MULUNGU anditsogolera,
Ndapumula m’mtimamo;
Ayang’anira njira zanga
Nsiku zanga zonsezo.

Mulungu anditsogolera
Nsiku zanga zonsezo;
Ndidzatsatira Mbuye wanga
M’njira mwake momwemo.

Masiku ena pali mdima,
Ndivutidwa m’mtimamo;
Masiku ena ndikondwera
Ndi zabwino zangazo.

Masiku onse m’mtima mwanga
Ndili ndi mtenderewo,
Chifukwa ndimakhulupira
Mtsogoleri wangayo.

Post navigation

Previous: Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
Next: Hymn 248 M’MENE ine ndisauka

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version