Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
Next: Hymn 239 TILI ndi mtendere

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version