Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
Next: Hymn 239 TILI ndi mtendere

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version