Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

 

TIYAMIKE Ambuye,
Chifukwa chotilola,
Kulowa m’chaka chino m’tisunge;
Sitingathe ‘fe tokha,
Kuyenda m’chaka chonse;
Ambuye m’titsogoze,
M’tisunge.

M’tisunge, m’tisunge,
Yesu tikupemphani m’tisunge;
Ife timalephera kuyenda m’njira tokha;
Yesu tikupemphani m’tisunge.

Dziko lapansi pano timangoyenda chabe,
Wosaganiziranso za moyo;
Timaganiza kuti moyowu sudzathanso,
Ambuye m’tikumbutse leroli.

Moyowu ngwapafupi, monga kugwa kwa tsamba,
Monga kumanga mtolo m’tisunge;
Ambuye m’tidalitse,
Nthawi isanafike;
Kuti tingataike m’tisunge.

Post navigation

Previous: Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
Next: Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version