Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 405 POLENGA dzikoli

  1. Home   »  
  2. Hymn 405 POLENGA dzikoli

Hymn 405 POLENGA dzikoli

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 405 POLENGA dzikoli

 

POLENGA dzikoli
Pakumva Inudi,
Kwayeratu;
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo
Palibe mawuwo,
Muŵaletu.

Inu wakudzatu
Kuŵachiritsadi
Anthendawo,
Kupatsa moyowo,
Kuona m’masomo,
Pa anthu onsewo
Muŵaletu.

Mzimu woonadi
Ndi wachikondicho,
Idzanitu;
Muunikirepo
Pali zamdimazo,
Pa dziko ponsepo
Muŵaletu.

Inu atatuwo,
Wodala Mlunguyo,
Timveretu;
Pa dziko ponsepo
Muchotse mdimawo,
Mutume Mawuwo,
Muŵaletu.

Post navigation

Previous: Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Next: Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version