Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 405 POLENGA dzikoli

  1. Home   »  
  2. Hymn 405 POLENGA dzikoli

Hymn 405 POLENGA dzikoli

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 405 POLENGA dzikoli

 

POLENGA dzikoli
Pakumva Inudi,
Kwayeratu;
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo
Palibe mawuwo,
Muŵaletu.

Inu wakudzatu
Kuŵachiritsadi
Anthendawo,
Kupatsa moyowo,
Kuona m’masomo,
Pa anthu onsewo
Muŵaletu.

Mzimu woonadi
Ndi wachikondicho,
Idzanitu;
Muunikirepo
Pali zamdimazo,
Pa dziko ponsepo
Muŵaletu.

Inu atatuwo,
Wodala Mlunguyo,
Timveretu;
Pa dziko ponsepo
Muchotse mdimawo,
Mutume Mawuwo,
Muŵaletu.

Post navigation

Previous: Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Next: Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version