Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

 

M’MENE umauka m’maŵa,
Sunagwire ntchitozo,
Sunayambe kukayenda,
Ugwadire Mlunguyo.
Pena uli kusekera,
Pena nkhaŵa m’mtimamo,
Wachimwemwe, wachisoni,
Uza Yesu zonsezo.

Wakuchezacheza naye
Ukagwira ntchitozo;
Pakukumbukira Yesu,
Nkhaŵa zidzachokanso
Ndi zapansi zikafuna
Kukudzaza m’mtimamo,
Utsogole kopemphera,
Uza Yesu zonsezo.

Ndi m’kutero udzadziŵa
Chifuniro chakecho; Iye adzakuthandiza
Uthangate enanso:
Ndi ofoka ulimbitse,
Akulapa bwezatu;
Ndi za ntchito zake izi
Uza Yesu zonsezo.

Ndipo ngati ungolema,
Ulefuka m’dzulomo,
Ndi Satana akayesa
Kukukola m’mtimamo:
Wakufoka, wakuopa,
Penyetsetsa Iyeyo;
Udzakhazikika m’mtima
Pakumuza zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 405 POLENGA dzikoli
Next: Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version