Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

  1. Home   »  
  2. Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

 

MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.

Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!

Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!
Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kwa Inu ulemu.

Post navigation

Previous: Hymn 427 AULENDO amayenda
Next: Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version