Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,

 

TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
Yakuyamika Mbuye wathuyo;
Mtendere wake tiufunadi,
Titapemphera tinke kwathuko.

Titanka kwathu mkhale nafeko,
Tikufunani Yesu Mbuyathu;
Musunge ife nthaŵi zonsezo,
Mutiyeretse m’mtima mwathu mbuu!

Usiku uno mutisungedi,
Khalani m’fupi m’nyumba mwathumo;
Mamaŵanso mudzatidzutse nji!
Kuti tigwire ntchito zathuzo.

Mtitsogolere nthaŵi zonsezo;
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo,
Sitidzaopa kanthu kena ’yi.

Post navigation

Previous: Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
Next: Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 972 Akristu limbikani,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version