Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

 

MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m’mtendere;
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje;
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi dziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Ndithudi tadala;
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mphatso zaulere;
Nkhalango, madambo abwino,
Ngwokoma Malaŵi.

O! Ufulu tigwirizane
Kukweza Malaŵi;
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire;
Pankhondo nkana pa mtendere
Cholinga n’chimodzi,
Mayi, Bambo, tidzipereke
Pokweza Malaŵi.

Post navigation

Previous: Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
Next: Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 169 M’manda nagonamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version