Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

  1. Home   »  
  2. Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

 

KONZA mtima iwe mbale,
Pakuleka tchimo;
Siya zonse uzikonda,
Ndikutsata Yesu.

Konza mtima wako lero,
Yesu alowemo;
Ndipo usachedwe iwe,
Taata Yesu lero.

Imva kuyankhula kwake,
Mawu a chikondi;
Ayankhula iwe lero,
Kuti upumule.

Nthawi ya chisomo m’dziko,
Ndi inotu mbale;
Yom’dziwatu Mpulumutsi,
Ukali ndi moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
Next: Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version