Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 315 YENDANI munjira yake,
Next: Hymn 317 UKATHA moyo wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version