Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 315 YENDANI munjira yake,
Next: Hymn 317 UKATHA moyo wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version