Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

  1. Home   »  
  2. Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

 

KUDZA kwa Mbuye
kudzatero monga mphenzi,
Ing’anima M’mwamba choncho Iye,
Dziko lidzanjenjemera oyipa onse,
Nayamba kuthawa powona Iye.

Yesu akhala pampando,
Kuweruza makamuwo;
Nkhosa dzanja lamanjalo,
Mbuzi kudzanja lamanzelero.

Ayimba kumpando’ko wolemekezeka,
Mfumu ya Kumwamba
Mbuye Yesu,
Alira m’Gehenamo moto, moto, moto,
Ndipeze kuti madzi akumwa.

Udzachitanji mbale pobwera Ambuye,
Kudzaweruza dziko lapansi,
Ngati sudakonzeke khulupira Yesu,
Kuti upeze moyo wosatha.

Post navigation

Previous: Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version