Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

  1. Home   »  
  2. Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

 

MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Ndikhale munda wanu wakupatsa
Zipatso zoyenera Mbuyeyo.

Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
Chikondi chanu chija chachikulu;
Lembani mawu anu pamtimanga,
Kuti ndikhumbukire zanuzo.

Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.

Wotsogolera, munditsogolere
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate,
Nditsate Yesu ndikuyendayenda
M’njira yomweyo anapondamo.

Mthandizi ndinu, mndithangate ine
Kupempha bwino izo zindisoŵa.
Kupempha monga Mlungu amafuna
Kulingalira zake zokhazo.

Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense,
Mundichitire ntchito yaikulu;
Mtima woyera ndi womvera mpatse,
Wodzala ndi chikondi chanucho.

Post navigation

Previous: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
Next: Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version