Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

 

MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
Mufike nazo mphamvu zanu zazikuluzo.

Mufike monga nyali younika m’mtimamo.
Mutidziŵitse zakuipa zakukhalamo.

Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
Mutiyeretse ifetu m’mitima mwathumo.

Mufike monga ngati njiŵa yamtenderewo.
Kutitu anthu anu onse akondanetu.

Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
Tikhale tonse nazo mphamvu zanu zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version