Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

  1. Home   »  
  2. Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

 

AMBUYE ngwodalitsika,
Mulungu wa Israyeli ndiye,
Poti anayang’ana naŵawombola anthu ake,

Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake;
Monga analankhula mwa aneneri ake,

Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida,
Ndipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni.

Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija,
Ndi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu,

Choti timtumikire osaŵaopa ’dani athu,
Ndi kuyeranso mtima mwa chilungamo nsiku zonse.

Mwana, adzakuyesa mneneritu wa Wamkulukulu,
Ndiwe udzakonzera njira ya Mbuye Wakumwamba.

Udzadziŵitsa anthu za Mpulumutsi wawo yemwe
Aŵakhululukira
Nafafaniza tchimo lawo,

Poti Mulungu wathu ali ndi mtima wachifundo.
Ndiye kumwamba komwe
Ationetsa mbanda kucha,

Poŵalitsira omwe ali mumdima ndi muimfa,
Ndi potilunjikitsa tonse munjira yamtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
Next: Hymn 29 CHIKONDI cha

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version