Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

 

MAWU akewo anamveka ponse,
Olalikidwa ndi aneneriwo;
Kuti yense wakumvera mawuwo,
Apulumuke.

(Mawuwo) Amveke,
(Tu) Kwa onsewo;
(Wo) Muetseratu ‘we sadzafa ndithu.

Tamveratu ‘we Mawu a Mulungu,
Khulupilira mwa
Ambuye Yesu;
Udzalandira moyo wosathawo,
Udzakondwera.

Tsoka kwa iye wosakhulupira,
Zolalikidwa ndi aneneriwo;
Koma patsiku la chiŵeruziro,
Adzafa ndithu

Post navigation

Previous: Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
Next: Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version