Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
Next: Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1612 Adzadza indetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version