Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
Next: Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version