Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

  1. Home   »  
  2. Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

 

ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
Ambuye wa Kumwambako aloŵe momwemo.

Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
Kufana ndi nyenyezi younika m’mdimamo.

Ankondo a Mulungu ’nu,
Yendani m’njiramo,
Mitima yanu yonseyo iyeretsedwe mbuu!

Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
Mlaliketu Uthenga kwa anthu onsewo.

Musamaopa kanthu ’yi tamani Yesuyo;
Kaimbireni nyimboyi ndi mphamvu zonse.

Zipata zatsegudwa mbee! za m’dziko monsemo;
Ambuye wapambanatu ndi mtanda wakewo.

Post navigation

Previous: Hymn 412 MOYO uli pafupi,
Next: Hymn 414 INU bambo, inu mayi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version