Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

 

YEHOVA Mlungu wathu,
Amene mumapatsa
Zipatso za chikondi
Polenga anthu anu,
Mupatse awa ‘ŵiri
Mitima yokondwetsa,
Yofana m’munda muja
Munayendamo kale.

Mbuyathu wokondedwa,
Pokhala m’dziko muno
Munadza ku ukwati,
Naŵadalitsa onse;
Ukwatiwu mukonze,
Mukhale nafe pano;
Iwowa m’ŵadalitse
M’chifundo chanu chonse.

Ndi Mzimutu Woyera
Mufike nayo mphamvu,
Mukatsangane nawo
Akupangana omwe;
Mupatse ’wo chisomo
Chokometsetsa mtima;
Chikuletu chikondi
Chitsazo nchanu chomwe.

Mulungu mwa Atatu,
Atate, Mwana, Mzimu,
Tikhaletu wokondwa
Ndi Inu m’chiyanjano;
Titama Inu Mlungu,
Wokonda ife ndinu;
M’ulendo wathu wonse
Tiyende m’chikondano.

Post navigation

Previous: Hymn 435 ANAKWATIRA kale
Next: Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version