Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

  1. Home   »  
  2. Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 443 M’MAŴA tizifesa

 

M’MAŴA tizifesa
Mbewu zakukoma,
Msana ndi usiku
Tizifesa momwe.
Nyengo yamasika
Tidzatema m’munda,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Ndi zipatsozo
Ndi zipatsozo
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tizifesa m’dzuŵa
Tizifesa m’mthunzi,
Sitiopa ife
Mtambo ndi chisanu.
Athatu masika
Ntchitozi zidzatha;
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Tingolira kaya,
Koma tidzafesa
Mbewu za Ambuye;
Ntchitoyo nja Yesu.
Adzachotsa msozi,
Adzatilandira,
Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.

Post navigation

Previous: Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
Next: Hymn 444 YEMWE afesa nalira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version