Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

 

IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Zachisautso chomwechili nkudza;
Cha nambala ya a sikisi atatu;
Kodi tidzapiliradi?

Kodi inu mayi mudzapiliradi
Kuyenda inu wausiwa.
Kodi inu bambo mudzapiliradi
Panthawi ya masautsowo?

Zizindikirozo zili kuwoneka,
Kutitu nkhondoyo yayandikadi;
Tisakhaletu odabwitsika konse,
Tilimbike kupemphera.

Tidzawona ena a ifetu zedi,
Tili kudindidwa pamphumi pathu;
Tidziwetu kuti sitinalembedwe,
Mayina m’buku mulibe.

Post navigation

Previous: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
Next: Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version