Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

  1. Home   »  
  2. Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

 

POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
Matenda, imfa ndi usiwa;
Moyo umalefuka,
Ndikugwetsedwa mphwayi;
Mpaka nditamuuza Yesuyo.

Um fotokozere Yesu vuto lako,
Um fotokozere Yesu zonsezo;
Um’fotokozere Yesu vuto lako;
Adzakuchitira chifundo.

Pokumana m’mayesero a dziko lino,
Ndinasokera kutaliko;
Yesu nandigwira dzanja,
Nanditsogolera;
Mmene ndinamuuza zonsezo.

Abale tisachedwe ndi za dziko lino,
Za dziko lino ndi zachabe;
Yesu akufuna tibwere kwa Iye lero,
Kuti timuuzetu zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 296 TIYENI Akhristu,
Next: Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version