Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

 

TIMVE za anamwali khumi,
Okonzeka mosiyana;
Asanu anali opusa zedi,
Ena anachenjeradi.

Asanu anatenga mafuta padera,
Iwowa anachenjera,
Asanu sanatenge mafuta adera,
Iwowa anapusadi.

Mkwati pamene anafika,
Pakati pa usikuwo,
Asanu osatenga mafutawo,
Sanathe kulowa m’nyumba.

Tisakhale ngati opusa,
Osatenga mafutawo.
Tikhale ngatitu ochenjerawo,
Titenge mafuta athu.

Mbale ukhale wochenjera,
Pakulapa zoipazo;
Pakukhulupiliratu Mulungu,
Kuti tikalowe M’mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
Next: Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version