Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

 

YESU ndiye Mbuye wanga,
Ndamva mawu akewo;
Anandilandira ine,
Nandipulumutsatu.

Mwalembedwa mukalata,
Mawu ake omwewo;
Kuti iwo akumvera,
Akalandiridwatu.

Ndinakhala woipadi,
Ndinam’kana kalelo;
Koma Yesu waiwala,
Mphulupulu zangazo.

Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu;
Mawu ake olembedwa,
Mukalata mwakemo.

Mumvetu abwenzi athu,
Musakanilire’yi;
Yesu ayitana inu,
Zalembedwa zomwezi.

Post navigation

Previous: Hymn 239 TILI ndi mtendere
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version