Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
Next: Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version