Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
Next: Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version