Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

  1. Home   »  
  2. Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

 

MUBWERE Mzimu Inu
Woyera, wakufatsa,
Muchotse mdima m’mtima mwathu
Tikapenye m’maso.

Mtisangalatse m’zonse,
Ndi wachifundo Inu,
Tiyembekeze kumapazi
A Mbuyathu Yesu.

Mtitsitsimutse ife
Kuchotsa nkhaŵa zathu,
Muyatse moto wachikondi
Mu mitima yathu.

Mtitsutse titachimwa
kutilapitsa m’mtima,
Mwonetsenso chikondi chokhululukira tchimo.

Kutiyeretsa m’mtima
Ndi ntchito yanu yokha,
Kupatsa moyo watsopano
M’mene timafoka.

Mukhale m’kati mwathu,
Mutichotsere mantha,
Tidzayamika ’Tate wathu,
Mwana wawo ndi ’Nu.

Post navigation

Previous: Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Next: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version