Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
Next: Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hello world!
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version