Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
Next: Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version