Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
Next: Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version