Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

 

KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Kunthawi zosatha;
Komwe kulibe mdima bii,
Yesu ndiye nyaliyo.

Mtandawo tidzasenza,
Korona tidzavala,
Pamodzi ndi oyera,
M’dziko la Kumwambako.

Chikondi chake cha Mlengi wathu,
Natuma Yesuyo;
Kudzatifera tonsefe,
Ndikutipatsa moyo.

Mulitu ulemelero M’mwamba,
Kwa anthu omvera;
Omwe akonda Yesuyo,
Ndikugwira ntchitoyo.

Post navigation

Previous: Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Next: Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version