Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
Next: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version