Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
Next: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version