Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
Next: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version