Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

  1. Home   »  
  2. Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

 

TIYENI, dzalireni nane,
Tidze ku mtanda wa Ambuye,
Tionse tichitetu maliro;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Kodi misozi itisoŵa,
Poona anthu amanyoza?
Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Anena mawu m’mtanda momwe
Mawu ochepa achifundo,
Apempherera ’dani ake;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Ona chikondi cha Mulungu,
Ona zoipazo za anthu,
Koma chakula ndi chikondi;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Post navigation

Previous: Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
Next: Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version