Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

 

MMENE Yesu adzabwera,
Adza ndi mitambo;
Ndipo diso lililonse,
Lidzamuwona Iye.

Adza, adza,
Adza ndi mitambo,
Ndipo diso lililonse;
Lidzamuwona Iye.

Adzakhala pa chimpando,
Choweruziracho;
Nadzayamba kuweruza,
Milandu ya anthu’fe.

Angelo ‘dzagwira ntchito,
Yolekanitsadi;
Anthu onse a padziko,
M’magulu awiritu.

Olugama nadzayima,
Kudzanja lamanja;
Koma onse oyipawo,
Mbali yakumanzere.

Akudzanja lamanjalo,
Kumoyo wosatha;
Akudzanja lamanzere,
Kumoto Wosathawo.

Post navigation

Previous: Hymn 76 E, MOYO wanga’we
Next: Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version