Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

 

ALINKUDZA wansoni Munthu,
Wakukhala Kumwamba;
Alinkudza m’ulemerero,
Ndi Mwamuna wa mtanda.

Aleluya, Aleluya,
Alinkudza kwa ife;
Ndi chimwemwe
Tidzamkomana,
Pakufika Ambuye.

Alinkudza Ambuye Yesu,
Wakuphedwa pa dziko;
Alinkudza kukhala Mfumu,
Yoweruza mayiko.

Pakufika asonkhanitsa,
Anthu ake oyera;
Adzafuna mitundu yonse,
Omwe Iye ‘nafera.

Post navigation

Previous: Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
Next: Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version