Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 356 YESU Mbuye onani,

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 356 YESU Mbuye onani,

 

YESU Mbuye onani,
Tadza poyitana Inu;
M’dzina lanu tifika,
Osekera kwa Atate.
M’khale nafe Inu nokha,
Tikayimba n’kupemphera.

Mbuye, Mzimu Woyera,
Munapatsa ana anu;
Kukalonga mumtima,
Mawu ndipo mvano womwe.
Zinthu zonse pansi pano,
Sizikondweretsa ife.

Mzimu, m’longe m’mtimamo,
Maphunziro achifundo;
Timve lero ndi mawa,
Ndi masiku onse: Yesu!
Ndipo M’mwamba tidzawona,
Tidazimva pansi pano.

Post navigation

Previous: Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
Next: Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version