Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

 

M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
Ndiyenderane nanu;
E, nditsamire pa ‘nu Yesu,
Panjira yonseyi.

Ndiwonetsere kuunika,
Kokoma kwanu Yesu!
Yabwino mbiri ndibukitse,
Yokondweretsayo.

Chitsime chakuyera ine,
Ndifananetu nacho;
Mundigwiritse ntchito zanu,
E, zanu zokhazo.

Mulamulire mtima, Yesu,
Ndi chifuniro changa;
Mulowe mwanga ngati Mfumu;
Kuti ndimvere ‘Nu.

Ndimamva njala kuno, Yesu,
Yakufunitsa Inu;
Kumwamba kwanu ndikukhumba.
Kukondwa nanuko.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version